28/08/2024
Lets fixing our community and villages Anthu mamidzimu ndmadelamu akuvutika not bcoz of only government aiii sanje kmaso kuipa ntima kwa Anthu ena mamidzimu kukukolezela uphawi madele ndmamidzimu tatiyen tidzikondana ndkufunila zabwino ngat amalawi ndpo tidzatukuka osadikilaso boma wina akamalimbikra tiyen tithandzane naye kaya akugulitsa malonda tiyen timugule k*t moyo wake udzipta chitsogolo ngat sitingasinthe kaganizidwe uphawi udzakhala bwez lathu ngat dziko stop fighting one another lets fighting with poverty πππ sanje kaduka dzimapha stop it may God bless our beloved malawi π²πΌπ²πΌπ²πΌ