22/07/2026
Munthuyu ndamupeza , ndacheza naye ndipo wapereka chidwi kwambiri. Akudziwa zambiri za vision ya UTM. Munthuyu amapanga kabaza ndiye ndimati timugulire Njinga yamoto . A UTM anzanga omwe mukumva mu mtimamo ngati ine tiyeni tikambilane ku inbox kuti tione kuti tipanga bwanji .
Mwadzuka bwanji abale anga a UTM party. Dzulo tinakwanitsa kusonkha K1,026,000 ndipo mmawa wa lero ndinapita ku shop kukaona njinga.
Mwachisomo cha Ambuye ogulitsa atichotsela ntengo kuchoka pa K2,950,000 kufika pa K2,850,000. Chotelo, tapereka deposit ndalama yonse yomwe mwapereka dzulo ndipo tatsala ndi balance ya K1,824,000. Ndipezeni ku Inbox , omwe mukufuna kuponya . Ambuye akudalitseni .
Chinthu ichi achiyambisa ndi a Hon Felix Ndawala. Tiyeni tigwirane nawo manja.