31/05/2026
Matthew 24:24 -
ⓙchifukwa Akhristu onama adzauka, ndi aneneri onama nadzaonetsa zizindikiro zazikulu ndi zozizwa: kotero kuti akanyenge, ngati nkotheka, osankhidwa omwe. Onani ndakuuziranitu pasadafike.
| For false christs and false prophets will rise and show great signs and wonders to deceive, if possible, even the elect.