27/09/2024
Gulu la anamwino omwe ndi akuno ku Malawi koma amagwira ntchito ku United Kingdom(Malawian-UK Nurses Association) likusonkhanitsa ndalama zoti zikagwiritsidwe ntchito ku chipinda chodikilira odwala ku Kamuzu Central. Cholinga chenicheni ndikuonjezera mabedi kuti akwane 50 komanso kugura zipangizo zina zofunikira.
Ngati mukufuna kudziwa zambiri imbani phone pa manambala awa:
Patrick Vundule +4471817118050
Rita Salika: +447881981114
Chisomo Adu: +447341448508
Daina Nthakomwa: +265883657069