Elder Dignity Malawi - EDIMA

Elder Dignity Malawi - EDIMA Elder Dignity Malawi is a non-profit organisation aimed at Promoting dignity, safety, and respect for the elderly in Malawi.

We raise awareness, prevent abuse, and protect our elders.

23/11/2025

Mudzi omwe umasamalira achikulire umayenda nkuunika kwa Mulungu.

Achikulire ndi mdalitso.

M’busa Pilira Chibwana wa mpingo wa Mulunguzi community akutikumbutsa kuti kusamalira achikulire si ntchito yosiyirana koma ndi udindo omwe Mulungu anaupereka kwa ife tonse.

Osazunza achikulire, osaphweketsa Hipapu.
21/11/2025

Osazunza achikulire, osaphweketsa Hipapu.

20/11/2025
Kodi mukudziwa?Mu Chaka cha 2025 chokha, achikulire oposa 18 aphedwa kamba koganiziridwa kuti ndi afiti mdziko la Malawi...
18/11/2025

Kodi mukudziwa?

Mu Chaka cha 2025 chokha, achikulire oposa 18 aphedwa kamba koganiziridwa kuti ndi afiti mdziko la Malawi.

Tiyeni tonse tigwirane manja pothana ndi mchitidwewu.

17/11/2025

“The glory of the elderly is their insight, their knowledge, and their wisdom.”

– Lailah Gifty Akita

Address

Zomba

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Elder Dignity Malawi - EDIMA posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Share