Ndife Amodzi

Ndife Amodzi Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from Ndife Amodzi, Nonprofit Organization, Area 58, Lilongwe.

Ndife Amodzi ("We Are One") is a community-led collective from neighborhoods like Mtandire, Mtsiliza, and Mwenela, dedicated to uplifting those in hardship through compassionate support and mutual aid

BUNGWE LA NDIFE AMODZI LERO PA 19 JULY, LIMAGWA UFA WA CHIMANGA KOMANSO UFA WA SOYA KWA AZIMAI OSAWA 32,KOMANSO LINAKWAN...
19/07/2026

BUNGWE LA NDIFE AMODZI LERO PA 19 JULY, LIMAGWA UFA WA CHIMANGA KOMANSO UFA WA SOYA KWA AZIMAI OSAWA 32,KOMANSO LINAKWANITSA KUENDELA CHEMWALI MOUREEN A KWAPIASANI OMWE AKUDWALA MWA PAKANTHAWI .

NDIPO BUGWELI LATHANDIZA SISTER MOREEN NDI KATUNDU OKWANA NDALAMA K30,000 KOMANSO NDIKUWAPATSA K70,000 PA MANJA.

ADMINISTRATION IKUTHOKOZA MA MEMBALA AWO CHIFUKWA CHA KUZIPELEKA KWAO POTI THANDIZOLI LIMACHOKELA PA KUTOLERA LIMODZI LIMODZI KWA MA MEMBALA AGULULI.AMBUYE AZIONJEZELA POMWE TIMACHOTSAPO AMEN!

11/06/2026

Ndi khumbo lathu kuti bungwe lathu la limodzi limodzi, lidzafike pomathandiza angakhale ma situation ngat awa,omwe azathu ena omwe tili nawo mu dziko la South African akusamalidwa ndi ma Gift givers komwe kwakhazikitsidwa ngat camp 🏕.

Tisadziyang'anile pansi,we can do this ,mwina sitingakhale ife mwina azitsogoleri ena dzaka zikubwelazi azachita,sitikuchemelera mavuto ai koma tiyeni tigwire limodzi ntchito zachifundo zimafunikila pa nyengo ngat imeneyi.
NDIFE AMODZI GROUP IN NTANDILE, AREA 56.

08/06/2026

MINUTES OF THE NDIFE AMODZI GROUP MEETING
• *Date* : 7 June 2026
• *Time* : 4:00 PM
• *Venue* : Kunyumba kwa a Kachere

*Opezekapo: Mamembala Omwe Analipo*
1. Anastanzia Kachere
2. Charity Chipofya
3. Gift Malenga
4. Alinafe Mlotha
5. Chimwemwe Bester
6. Gracious Chipofya
7. Mr. Tsoka

*Zolinga za mu Gulu ndi Thandizo la Ma Membala (Social Welfare)*
•Ma members adakambirana mozama za kukhazikitsa dongosolo la kasamalidwe ka ma members, powona kuti monga gulu logwirizana, ndikofunikira kuthandizana pakachitika zinthu zadzidzidzi monga maliro komanso matenda.

•Zotsatirazi ndi zomwe zagwirizanidwa pokhudza kayendetsedwe ka dongosololi:
•Oyenerera Kuthandizidwa: Thandizoli liziperekedwa kokha kwa mamembala omwe ali active pazochitika za gulu amene azakhale kuti afeledwa ndi achibale omwe ndi makolo, ana a munthu ofeledwa kapena achibale cha pafupi).

Kulembetsa kuti umembala ukhale wovomerezeka, gulu lakhazikitsa ndalama zolembesera u membership fee 1,000 ndi 1,000 yopelekedwa pa mwenzi

*Kapezedwe ka Ndalama:* Ndalama zothandizira mamembala zizitengedwa mwandondomeko m’thumba la ndalama zolembesera komanso zoyendetsera umembala.

*Chipepeso cha Maliro:* Ngati membala yemwe ali m'gulu wakumana ndi zovuta monga maliro, gululi lizipereka ndalama zokwana MK 20,000 zochokera m'thumba la chithandizoli kuti zithandizire pa maliro.

*Thandizo la Matenda/Kugonekedwa Chipatala* : Membala akadwala, gululi lizipatula MK 10,000 yoti yomuthandizila.

_Chonde tikuyenela kuziwa kuti apa ndi poyambila chabe pa gulu ngati kuli kusintha kuli konse gulu lizawuzidwa ndipo izi zapelekedwa kuwonaso mmene ma members omwe tili nawo ngati gulu_

*Komiti ya Chithandizo (Welfare Committee):* Zidagwirizana kuti pakufunika kusankhidwa Mtsogoleri kapena Komiti ya Chithandizo yomwe iziyang'anira komanso kuyendetsa bwino dipatimentiyi.

2. *Kugwirizana ndi Mafumu/Atsogoleri a m'Dera*
Gululi lidakambirana za kulimbitsa ubale ndi atsogoleri a m'derali ndipo lidagwirizana zokayendera atsog

08/06/2026

MINUTES OF THE NDIFE AMODZI GROUP MEETING
• *Date* : 7 June 2026
• *Time* : 4:00 PM
• *Venue* : Kunyumba kwa a Kachere

*Opezekapo: Mamembala Omwe Analipo*
1. Anastanzia Kachere
2. Charity Chipofya
3. Gift Malenga
4. Alinafe Mlotha
5. Chimwemwe Bester
6. Gracious Chipofya
7. Mr. Tsoka

*Zolinga za mu Gulu ndi Thandizo la Ma Membala (Social Welfare)*
•Ma members adakambirana mozama za kukhazikitsa dongosolo la kasamalidwe ka ma members, powona kuti monga gulu logwirizana, ndikofunikira kuthandizana pakachitika zinthu zadzidzidzi monga maliro komanso matenda.

•Zotsatirazi ndi zomwe zagwirizanidwa pokhudza kayendetsedwe ka dongosololi:
•Oyenerera Kuthandizidwa: Thandizoli liziperekedwa kokha kwa mamembala omwe ali active pazochitika za gulu amene azakhale kuti afeledwa ndi achibale omwe ndi makolo, ana a munthu ofeledwa kapena achibale cha pafupi).

Kulembetsa kuti umembala ukhale wovomerezeka, gulu lakhazikitsa ndalama zolembesera u membership fee 1,000 ndi 1,000 yopelekedwa pa mwenzi

*Kapezedwe ka Ndalama:* Ndalama zothandizira mamembala zizitengedwa mwandondomeko m’thumba la ndalama zolembesera komanso zoyendetsera umembala.

*Chipepeso cha Maliro:* Ngati membala yemwe ali m'gulu wakumana ndi zovuta monga maliro, gululi lizipereka ndalama zokwana MK 20,000 zochokera m'thumba la chithandizoli kuti zithandizire pa maliro.

*Thandizo la Matenda/Kugonekedwa Chipatala* : Membala akadwala, gululi lizipatula MK 10,000 yoti yomuthandizila.

_Chonde tikuyenela kuziwa kuti apa ndi poyambila chabe pa gulu ngati kuli kusintha kuli konse gulu lizawuzidwa ndipo izi zapelekedwa kuwonaso mmene ma members omwe tili nawo ngati gulu_

*Komiti ya Chithandizo (Welfare Committee):* Zidagwirizana kuti pakufunika kusankhidwa Mtsogoleri kapena Komiti ya Chithandizo yomwe iziyang'anira komanso kuyendetsa bwino dipatimentiyi.

2. *Kugwirizana ndi Mafumu/Atsogoleri a m'Dera*
Gululi lidakambirana za kulimbitsa ubale ndi atsogoleri a m'derali ndipo lidagwirizana zokayendera atsog

Send a message to learn more

Restoring hope for every home
05/06/2026

Restoring hope for every home

Address

Area 58
Lilongwe

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Ndife Amodzi posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Shortcuts

Share